MVUNGUTI BOOKS
Mvunguti Books, sister to the Kachere Series, publishes books in the many languages of Malawi, and since English has become one of them, it is not excluded either. While most of the teaching of theology in Malawi is done in English, most of the preaching, singing and praying is done in the many different languages of Malawi, so the Mvunguti Books intend to develop vernacular theology in Malawi and also to publish cultural texts.
     
 

SANGAYA: Mtsogoleri wa Sinodi ya Blantyre Mpingo wa CCAP
Silas S. Ncozana
Text in Chichewa
Mmodzi mwa atsogoleri a mpingo wodziwika kwambiri pa nthawi imene dziko lino limalandira ufulu wodzilamulira anali Mbusa Jonathan Sangaya. Iyeyu analowa udindowa mlembi wamkulu wa Sinodi ya Blantyre mumpingo wa CCAP mchaka wa 1958 kulowa m'malo mwa Tom Colvin, ndipo anatsogoleradi mpingo mnthawi yonse yosintha ulamuliro. Bukuli lithandiza owerenga kudziwa zinthu za mbiri pa nthawiyo ndi kumva kusintha kwa utsogoleri, kuchoka kwa amishonale kupita kwa a Malawi.
ISBN 99908-16-350-2, Mvunguti Book No. 1, 2001

     
 

PA CHIYAMBI ANAWALENGA CHIMODZIMODZI
Janet Y. Kholowa ndi Klaus Fiedler
Text in Chichewa
Ambiri anatsimikizika kuti Baibulo limaphunzitsa kuti amuna azilamulira akazi. Bukuli lafufuza mozama mitu yoyambirira itatu ya buku la Genesis ndipo lapeza zosiyaniranatu ndi zimene anthuwa amaganizira: Pa chiyambi Mulungu anawalenga chimodzimodzi.
ISBN 9908-16-22-5, Buku la Mvunguti No. 2, 1999
For the English translation of this book please see: In the Beginning God Created Them Equal

     
  MOYO NDI UTUMIKI WA MBUSA NDI MAI MOUCHA WA PROVIDENCE INDUSTRIAL MISSION
Patrick Makondesa
Text in Chichewa
Mbiri ya Mpingo wa Providence Industrial Mission (PIM) ndi yodziwika kwambiri kupyolera mwamstogoleri wake woyamba Mbusa John Chilembwe amene anaphedwa m'chaka cha 1915. Dr. Daniel Malekebu ndi mkazi wake Flora analowa m'malo mwake m'chaka cha 1926. Bukuli likulongosola moyo ndi utumiki wa Mbusa Muocha ndi mkazi wake amene anatsatira Dr. Malekebu ndi mkazi wake (1971-1987).
ISBN 9908-16-31-X, Mvunguti Book No. 3, 2000
     
  NTHANTHI ZA CHITONGA ZA KUSAMBIZGIYA NDI KUTAULIYA
David Mphande
Text in Chitonga
Proverbs are a never-ending treasure of wisdom for any people. In this book, written entirely in Chitonga, David Mphande presents 200 proverbs and explores how each of them can be used in preaching and teaching.
ISBN 99908-16-36-0, Mvunguti Book No. 5, 2000
     
  MTUMWI PAULO NDI UDINDO WA AMAYI MUMPINGO
Janet Y. Kholowa ndi Klaus Fiedler
Text in Chichewa
Kuno ku Malawi nkhani yakulalikira kwa amayi mtchalitchi ili mkamwamkamwa. Ena amakana, ena amavomereza, onse amatsimikiza kuti amatsatila Baibulo. Bukuli lafufuza mozama zimene Mtumwi Paulo anachita ndi kunena zokhudza udindo wa amayi mu tchalitchi.
ISBN 9908-16-31-X, Mvunguti Book No. 6, 2001
     
  CHIKONZEDWE CHA MPINGO: Zosintha zazikulu za uzimu 1500-1650
Steven Paas
Text in Chichewa
Bukuli limafotokozera mbiri ya Nyengo ya Chikonzedwe cha Mpingo ku maiko a ku Ulaya m'zaka za 1500-1650. Nyengoyi inali nthawi ya kusintha kwakukulu imene inatsegula chitseko cha tsogolo latsopano, ndiponso nthawiyi inagwedeza anthu. Anthu anafufuza mafunso pa zovuta zambiri. Panthawiyi Mulungu anatumiza nthumwi za Mpingo wake, kuti zitsogolere anthu kuwerenga ndi kutsatira Baibulo. Ntchito ya Chikonzedwechi inatsitsimutsa Mpingo. Zaka zambiri zitatha, mipingo ya ku Ulaya, kudzera m'ntchito ya Mishoni, inabweretsa Baibulo ku Africa, komwe kunakhazikitsidwa Mipingo yambiri. Anthu amene akufuna kumva bwino Mbiri ya Mpingo ya ku Africa ayenera kudziwa Mbiri ya Chikonzedwechi. Ichi ndi cholinga chake cha bukuli.
ISBN 99908-16-47-6, Mvunguti Book No. 7, 2002
     
 

THE GOD OF LOVE AND COMPASSION: A CHRISTIAN MEDITATION ON AIDS
Martin Ott et al.
Editions are available in English, Chichewa, or Tumbuka text
Since the outbreak of the AIDS pandemic in Malawi (the first case was reported in 1985) the different churches have embarked on a remarkable number of activities in the field of awareness programs and home-based care programs, not to mention treatment of AIDS patients in hospitals. But AIDS is not only a social and medical problem. For Christians it is a challenge to their faith. With high respect we acknowledge how Malawian Christians practise love towards the neighbour in caring for the sick and burying the dead. Nevertheless, the popular understanding of the disease within the Malawian churches needs further support and theological instruction.
Kachere Series, 9 pp, 2000

 
   

Journals and African Languages books are only
available for order through
Kachere Series.

   

For book orders outside of Africa please contact
African Books Collective.

 


BACK
TO TOP

For orders within Africa contact
Kachere Series.

 

HOME | NEW | BOOKS | MONOGRAPHS | TEXTS | STUDIES | THESES | AFRICAN LANGUAGES |
OTHER PUBLICATIONS | EDITORS |
 CONTACT US | LINKS